Utumiki:Gawo 25 (B)

Mipatuko iwiri imeneyi (Shia ndi Sunni) ndiofanana muzikhulupiriro zokhudza Mtumiki (s.a.w.w). Onse amakhulupirira kuti Mtumiki ndi: - otumizidwa ndi Mulungu. - Mtumiki omaliza. - Munthu osankhidwa ndi Mulungu kudzaongola anthu.

Mipatuko iwiri imeneyi (Shia ndi Sunni) ndiofanana muzikhulupiriro zokhudza Mtumiki (s.a.w.w).
Onse amakhulupirira kuti Mtumiki ndi:
- otumizidwa ndi Mulungu.
- Mtumiki omaliza.
- Munthu osankhidwa ndi Mulungu kudzaongola anthu.

 

AttachmentSize
File 11601-f-chichwa.mp458.39 MB

Add new comment