Zionetsero za Husain(a) mu Quran 5

Zionetsero za Husain(a) mu Quran 5

 
 Mulungu akunena  kuti:
و إذا الموئودة سئلت * بأى ذنب قتلت   التكوير / 8 - 9
Nthawi  yomwe  ana  achikazi  omwe  amaikidwa  mmanda  amoyo  adzafunsidwa  kuti  ndichifukwa  chani  adaphedwa?
Imam  Swadiq (a)  adanena  kuti  aya  imeneyi  idatsikira  Imam  Husain (a).
Al’awalim,volume 15, tsamba 19.

Add new comment